Ezara 5:9 - Buku Lopatulika9 Pamenepo tinafunsa akulu aja ndi kutere nao, Anakulamulirani ndani kumanga nyumba iyi, ndi kutsiriza khoma ili? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pamenepo tinafunsa akulu aja ndi kutere nao, Anakulamulirani ndani kumanga nyumba iyi, ndi kutsiriza khoma ili? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono tidaŵafunsa atsogoleriwo kuti, ‘Kodi adakulamulani ndani kuti mumange Nyumba imeneyi ndi kutsiriza makoma ake?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndipo tinawafunsa atsogoleriwo kuti, “Anakulolezani kuti mumangenso Nyumbayi ndi kutsiriza makoma ake ndani?” Onani mutuwo |