Ezara 5:8 - Buku Lopatulika8 Adziwe mfumu kuti ife tinamuka kudziko la Yuda, kunyumba ya Mulungu wamkulu, yomangidwa ndi miyala yaikulu, ndi kuikidwa mitengo pamakoma, ndipo inachitika mofulumira ntchitoyi, ndipo inayenda bwino m'dzanja mwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Adziwe mfumu kuti ife tinamuka kudziko la Yuda, kunyumba ya Mulungu wamkulu, yomangidwa ndi miyala yaikulu, niikidwa mitengo pamakoma, nichitika mofulumira ntchitoyi, nikula m'dzanja mwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Inu mfumu, mudziŵe kuti ife tidaapita ku dziko la Yuda ku Nyumba ya Mulungu wamkulu. Nyumbayo ikumangidwa ndi miyala ikuluikulu, ndipo akuyalika mitengo pa makoma. Ntchito imeneyi ikuchitika mwachangu, ndipo ikuyenda bwino kwambiri poigwira anthuwo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Amfumu mudziwe kuti ife tinapita ku dziko la Yuda ku Nyumba ya Mulungu wamkulu. Nyumbayo ikumangidwa ndi miyala ikuluikulu ndipo akuyala matabwa pa makoma. Ntchitoyi ikugwiridwa mwachangu ndipo ikuyenda bwino kwambiri mwautsogoleri wawo. Onani mutuwo |