Ezara 5:6 - Buku Lopatulika6 Zolembedwa m'kalata amene Tatenai kazembe wa tsidya lino la mtsinjewo, ndi Setari-Bozenai, ndi anzake Afarisikai, okhala tsidya lino la mtsinje, anatumiza kwa Dariusi mfumu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Zolembedwa m'kalata amene Tatenai kazembe wa tsidya lino la mtsinjewo, ndi Setari-Bozenai, ndi anzake Afarisikai, okhala tsidya lino la mtsinje, anatumiza kwa Dariusi mfumu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Nayi kalata yomwe Tatenai, bwanamkubwa wa dera la Patsidya pa Yufurate, ndiponso Setari-Bozenai ndi anzake, akazembe omwe anali m'chigawo cha Patsidya pa Yufurate, adatumiza kwa mfumu Dariusi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iyi ndi kalata imene Tatenai bwanamkubwa wa dera la patsidya pa Yufurate, ndiponso Setari-Bozenai ndi anzake, akazembe amene anali mʼchigawo cha patsidya pa Yufurate, anatumiza kwa mfumu Dariyo Onani mutuwo |