Ezara 5:5 - Buku Lopatulika5 Koma diso la Mulungu wao linali pa akulu a Ayuda, ndipo sanawaletse mpaka mlandu unamdzera Dariusi, nabweza mau a mlanduwo m'kalata. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma diso la Mulungu wao linali pa akulu a Ayuda, ndipo sanawaletse mpaka mlandu unamdzera Dariusi, nabweza mau a mlanduwo m'kalata. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma Mulungu wao ankaŵasamalira atsogoleri a Ayuda, ndipo choncho anthu aja adaganiza zoti asaŵaletse Ayudawo kumanga mpaka atalembera mfumu Dariusi kalata, nkulandiranso yankho lake pa nkhani imeneyi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Koma Mulungu wawo amayangʼanira atsogoleri Ayuda, motero kuti anthu aja anaganiza kuti asawaletse kumanga Nyumbayo mpaka atalembera mfumu Dariyo kalata ndi kulandira yankho lake. Onani mutuwo |