Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 5:4 - Buku Lopatulika

4 Nanena naonso motere, Maina ao a anthu omanga chimangidwe ichi ndiwo ayani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Nanena naonso motere, Maina ao a anthu omanga chimangidwe ichi ndiwo ayani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Adaŵafunsanso kuti, “Kodi anthu amene akumanga Nyumba imeneyiŵa, maina ao ndani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Anawafunsanso kuti, “Kodi anthu amene akumanga nyumbayi mayina awo ndani?”

Onani mutuwo Koperani




Ezara 5:4
2 Mawu Ofanana  

Tinawafunsanso maina ao, kukudziwitsani, kuti tilembere maina a anthu akuwatsogolera.


Pamenepo anachita Bezalele ndi Oholiyabu, ndi anthu aluso, amene Yehova adaika luso ndi nzeru m'mtima mwao adziwe machitidwe ake a ntchito yonse ya utumiki wake wa malo opatulika, monga mwa zonse adauza Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa