Ezara 5:3 - Buku Lopatulika3 Nthawi yomweyi anawadzera Tatenai kazembe tsidya lino la mtsinjewo, ndi Setari-Bozenai, ndi anzao, nanena nao motere, Anakulamulirani inu ndani kumanga nyumba iyi, ndi kutsiriza khoma ili? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Nthawi yomweyi anawadzera Tatenai kazembe tsidya lino la mtsinjewo, ndi Setari-Bozenai, ndi anzao, nanena nao motere, Anakulamulirani inu ndani kumanga nyumba iyi, ndi kutsiriza khoma ili? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Nthaŵi yomweyo Tatenai, bwanamkubwa wa chigawo cha Patsidya pa Yufurate ndi Setari-Bozenai, pamodzi ndi anzao adapita kwa iwowo, ndipo adalankhula nawo naŵafunsa kuti, “Adakulamulani ndani kuti mumange Nyumba imeneyi ndi kumaliza khoma lake?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pa nthawi imeneyo Tatenai, bwanamkubwa wa chigawo cha patsidya pa Yufurate pamodzi ndi Setari-Bozenai ndi anzawo anapita kwa iwo ndi kukawafunsa kuti, “Anakulolani ndani kuti mumangenso Nyumba imeneyi ndi kutsiriza khoma lake?” Onani mutuwo |