Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 5:10 - Buku Lopatulika

10 Tinawafunsanso maina ao, kukudziwitsani, kuti tilembere maina a anthu akuwatsogolera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Tinawafunsanso maina ao, kukudziwitsani, kuti tilembere maina a anthu akuwatsogolera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Tidaŵafunsanso maina ao, kuti tikalemba maina a atsogoleri ao, tidzakudziŵitseni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Tinawafunsanso mayina a atsogoleri awo, kuti tikalemba mayina atsogoleriwo tidzakudziwitseni kuti muwadziwe.

Onani mutuwo Koperani




Ezara 5:10
3 Mawu Ofanana  

Natiyankha mau motere, ndi kuti, Ife ndife akapolo a Mulungu wa kumwamba ndi dziko lapansi, tilikumanga nyumba imene idamangika zapita zaka zambiri; inaimanga ndi kuitsiriza mfumu yaikulu ya Israele.


Nanena naonso motere, Maina ao a anthu omanga chimangidwe ichi ndiwo ayani?


Pamenepo tinafunsa akulu aja ndi kutere nao, Anakulamulirani ndani kumanga nyumba iyi, ndi kutsiriza khoma ili?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa