Ezara 5:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo aneneri, Hagai mneneriyo, ndi Zekariya mwana wa Ido, ananenera kwa Ayuda okhala mu Yuda ndi mu Yerusalemu; m'dzina la Mulungu wa Israele ananenera kwa iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo aneneri, Hagai mneneriyo, ndi Zekariya mwana wa Ido, ananenera kwa Ayuda okhala m'Yuda ndi m'Yerusalemu; m'dzina la Mulungu wa Israele ananenera kwa iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Nthaŵi imeneyo aneneri aŵa, Hagai ndi Zekariya mwana wa Ido, adayamba kulankhula kwa Ayuda okhala m'dziko la Yuda ndi mu Yerusalemu. Ankalankhula m'dzina la Mulungu wa Israele amene anali nawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Nthawi imeneyo aneneri Hagai ndi Zekariya, mwana wa Ido, ankayankhula kwa Ayuda okhala mʼdziko la Yuda ndi mu Yerusalemu mʼdzina la Mulungu wa Israeli, amene anali nawo. Onani mutuwo |