Ezara 4:8 - Buku Lopatulika8 Rehumu chiwinda cha malamulo, ndi Simisai mlembi, analemba kalata kwa mfumu Arita-kisereksesi, wakutsutsana naye Yerusalemu motere: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Rehumu chiwinda cha malamulo, ndi Simisai mlembi, analemba kalata kwa mfumu Arita-kisereksesi, wakutsutsana naye Yerusalemu motere: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Kenaka Rehumu Bwanamkubwa ndi Simisai mlembi wake, nawonso adalemba yao kalata kwa mfumu Arita-kisereksesi yoneneza anthu a ku Yerusalemu. Adalemba motere: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Rehumu mkulu wankhondo ndi Simisai mlembi, nawonso analemba kalata yawo yoneneza anthu a ku Yerusalemu kwa mfumu Aritasasita. Anayilemba motere: Onani mutuwo |