Ezara 4:4 - Buku Lopatulika4 Pamenepo anthu a m'dziko anafoketsa manja a anthu Ayuda, nawavuta pomanga, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pamenepo anthu a m'dziko anafoketsa manja a anthu Ayuda, nawavuta pomanga, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Atamva zimenezi anthu a m'dzikomo adayamba kutayitsa mtima Ayuda, ndi kuŵachititsa mantha kuti aleke ntchito yomangayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tsono anthu a mʼdzikomo anayamba kuchititsa ulesi anthu a ku Yuda, ndi kuwachititsa mantha kuti aleke ntchito yomangayo. Onani mutuwo |