Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 4:21 - Buku Lopatulika

21 Mulamulire tsono kuti anthu awa aleke, ndi kuti asamange mzinda uwu, mpaka ndidzalamulira ndine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Mulamulire tsono kuti anthu awa aleke, ndi kuti asamange mudzi uwu, mpaka ndidzalamulira ndine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Tsono inu mulembe lamulo loŵaletsa anthu amenewo kuti asamangenso mzinda umenewo, mpaka ine nditaloleza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Tsopano inu khazikitsani lamulo kuti anthu amenewo asiye ntchitoyo, asamangenso mzindawo mpaka ine nditalamula

Onani mutuwo Koperani




Ezara 4:21
2 Mawu Ofanana  

Panalinso mafumu amphamvu mu Yerusalemu amene anachita ufumu tsidya lija lonse la mtsinje, ndipo anthu anawapatsa msonkho, thangata, ndi msonkho wa m'njira.


Chenjerani mungadodomepo, chidzakuliranji chisauko cha kusowetsa mafumu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa