Ezara 4:16 - Buku Lopatulika16 Tili kudziwitsa mfumu kuti ukamangidwa mzindawu, nakatsirizidwa malinga ake, simudzakhala nalo gawo tsidya lino la mtsinjewo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Tili kudziwitsa mfumu kuti ukamangidwa mudziwu, nakatsirizidwa malinga ake, simudzakhala nalo gawo tsidya lino la mtsinjewo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tikukudziŵitsani inu amfumu kuti ngati mzinda umenewu aumanganso ndi kutsirizanso makoma ake, ndiye kuti inuyo simudzatha kumalamulirabe m'chigawo cha Patsidya pa Yufuratecho.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Tsono tikukudziwitsani amfumu kuti ngati mzinda umenewu umangidwanso ndi makoma ake nʼkutsirizidwanso ndiye kuti inu simudzalamuliranso chigawo cha patsidya pa Yufurate. Onani mutuwo |