Ezara 4:1 - Buku Lopatulika1 Atamva tsono adani a Yuda ndi Benjamini kuti ana aja a ndende analikumangira Yehova Mulungu wa Israele Kachisi, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Atamva tsono adani a Yuda ndi Benjamini kuti ana aja a ndende analikumangira Yehova Mulungu wa Israele Kachisi, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Adani a Yuda ndi a Benjamini adaamva kuti anthu obwerako ku ukapolo aja akumangira Nyumba Chauta, Mulungu wa Aisraele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Adani a Yuda ndi Benjamini anamva kuti anthu obwera ku ukapolo aja akumangira Nyumba Yehova, Mulungu wa Israeli. Onani mutuwo |