Ezara 3:7 - Buku Lopatulika7 Anaperekanso ndalama kwa amisiri a miyala, ndi a mitengo; ndi chakudya, ndi chakumwa, ndi mafuta, kwa a ku Sidoni, ndi a ku Tiro, kuti atenge mikungudza ku Lebanoni, kufika nayo ku nyanja ku Yopa, monga adawalola Kirusi mfumu ya Persiya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Anaperekanso ndalama kwa amisiri a miyala, ndi a mitengo; ndi chakudya, ndi chakumwa, ndi mafuta, kwa a ku Sidoni, ndi a ku Tiro, kuti atenge mikungudza ku Lebanoni, kufika nayo ku nyanja ku Yopa, monga adawalola Kirusi mfumu ya Persiya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono anthu adapereka ndalama kwa amisiri osema miyala ndi kwa amisiri a matabwa. Adatumiza chakudya, zakumwa ndi mafuta kwa anthu a ku Sidoni ndi ku Tiro, kuti azigulira mitengo ya mkungudza ya ku Lebanoni. Mitengoyo adafika nayo ku nyanja mpaka ku mzinda wa Yopa. Zonsezi ankazichita potsata chilolezo cha Kirusi, mfumu ya ku Persiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndipo anapereka ndalama kwa amisiri a miyala ndi kwa amisiri a matabwa, ndi chakudya, chakumwa ndi mafuta kwa anthu a ku Sidoni ndi a ku Turo, kuti abweretse mitengo ya mkungudza pa nyanja kuchokera ku Lebanoni mpaka ku Yopa. Zonsezi anachita malinga ndi chilolezo chimene analandira kuchokera kwa Koresi, mfumu ya Peresiya. Onani mutuwo |