Ezara 3:6 - Buku Lopatulika6 Chiyambire tsiku loyamba la mwezi wachisanu ndi chiwiri anapereka nsembe zopsereza kwa Yehova; koma sanamange maziko a Kachisi wa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Chiyambire tsiku loyamba la mwezi wachisanu ndi chiwiri anapereka nsembe zopsereza kwa Yehova; koma sanamange maziko a Kachisi wa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Kuyambira pa tsiku loyamba la mwezi wachisanunchiŵiri, adayamba kupereka nsembe zopserezazi kwa Chauta. Koma maziko a Nyumba ya Mulungu anali asanamangidwebe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kuyambira pa tsiku loyamba la mwezi wachisanu ndi chiwiri, iwo anayambanso kupereka nsembe zopsereza kwa Yehova, ngakhale kuti maziko a Nyumba ya Yehova anali asanamangidwe. Onani mutuwo |