Ezara 3:5 - Buku Lopatulika5 atatero anaperekanso nsembe yopsereza yosalekeza, ndi za pokhala mwezi, ndi za nyengo zoikika zonse za Yehova zopatulika, ndi za munthu yense wopereka nsembe yaufulu kwa Yehova mwaufulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 atatero anaperekanso nsembe yopsereza yosalekeza, ndi za pokhala mwezi, ndi za nyengo zoikika zonse za Yehova zopatulika, ndi za munthu yense wopereka nsembe yaufulu kwa Yehova mwaufulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pambuyo pake ankapereka nsembe zopsereza monga mwa nthaŵi zonse, nsembe zopereka pokhala mwezi ndi pa masiku onse achikondwerero oikidwa otamandira Chauta, kudzanso nsembe zaufulu zopereka kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pambuyo pake, ankapereka nsembe zopsereza, nsembe zopereka pa nthawi ya mwezi watsopano ndi za pa masiku onse a chikondwerero oyikidwa kutamandira Yehova, kudzanso nsembe zaufulu zopereka kwa Yehova. Onani mutuwo |