Ezara 3:1 - Buku Lopatulika1 Utakhala tsono mwezi wachisanu ndi chiwiri, ana a Israele ali m'midzimo, anthuwo anasonkhana ngati munthu mmodzi ku Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Utakhala tsono mwezi wachisanu ndi chiwiri, ana a Israele ali m'midzimo, anthuwo anasonkhana ngati munthu mmodzi ku Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pa mwezi wachisanu ndi chiŵiri, ana a Aisraele ali m'midzi mwao, anthu adasonkhana ku Yerusalemu ndi cholinga chimodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Utafika mwezi wa chisanu ndi chiwiri Aisraeli atakhala kale mʼmidzi yawo, anthu anasonkhana ku Yerusalemu ndi cholinga chimodzi. Onani mutuwo |