Ezara 2:6 - Buku Lopatulika6 Ana a Pahatimowabu, a ana a Yesuwa ndi Yowabu, zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi atatu kudza khumi ndi awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ana a Pahatimowabu, a ana a Yesuwa ndi Yowabu, zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi atatu kudza khumi ndi awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 A banja la Pahatimowabu, ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa ndi Yowabu, 2,812. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 zidzukulu za Pahati-Mowabu (zochokera kwa Yesuwa ndi Yowabu) 2,812 Onani mutuwo |