Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 2:41 - Buku Lopatulika

41 Oimba: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

41 Oimba: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

41 Oimba nyimbo anali aŵa: a banja la Asafu, 128.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

41 Anthu oyimba nyimbo anali awa: Zidzukulu za Asafu 128.

Onani mutuwo Koperani




Ezara 2:41
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Alevi anaika Hemani mwana wa Yowele, ndi a abale ake Asafu mwana wa Berekiya, ndi a ana a Merari, abale ao, Etani mwana wa Kusaya;


wakhumi ndi chisanu ndi chitatu Hanani, ana ake ndi abale ake khumi ndi awiri;


Ndi mbale wake Asafu wokhala ku dzanja lake lamanja, ndiye Asafu mwana wa Berekiya, mwana wa Simea,


Alevi: ana a Yesuwa, ndi Kadimiyele, ndiwo a ana a Hodaviya, makumi asanu ndi awiri mphambu anai.


Ana a odikira: ana a Salumu, ana a Atere, ana a Talimoni, ana a Akubu, ana a Hatita, ana a Sobai, onse pamodzi ndiwo zana limodzi mphambu makumi atatu kudza asanu ndi anai.


Ndipo pomanga maziko a Kachisi wa Yehova, amisiriwo anaimiritsa ansembe ovala zovala zao ndi mphalasa, ndi Alevi ana a Asafu ndi nsanje, kuti alemekeze Yehova, monga umo anaikiratu Davide mfumu ya Israele.


ndi Mataniya mwana wa Mika, mwana wa Zabidi, mwana wa Asafu, ndiye mkulu wakuyamba mayamiko, popemphera; ndi Bakibukiya wotsatana naye mwa abale ake, ndi Abida mwana wa Samuwa, mwana wa Galali, mwana wa Yedutuni.


Oimbira: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi anai kudza asanu ndi atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa