Ezara 2:41 - Buku Lopatulika41 Oimba: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Oimba: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Oimba nyimbo anali aŵa: a banja la Asafu, 128. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Anthu oyimba nyimbo anali awa: Zidzukulu za Asafu 128. Onani mutuwo |