Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 2:12 - Buku Lopatulika

12 Ana a Azigadi, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi awiri ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ana a Azigadi, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi awiri ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 A banja la Azigadi, 1,222.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 zidzukulu za Azigadi 1,222

Onani mutuwo Koperani




Ezara 2:12
4 Mawu Ofanana  

Ana a Bebai, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.


Ana a Adonikamu, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi mmodzi.


Ndi wa ana a Azigadi, Yohanani mwana wa Hakatani; ndi pamodzi naye amuna zana limodzi mphambu khumi limodzi.


Ana a Azigadi, zikwi ziwiri mphambu mazana atatu kudza makumi awiri ndi awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa