Ezara 1:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo onse akuwazinga analimbitsa manja ao ndi zipangizo za siliva, ndi golide, ndi chuma, ndi zoweta, ndi zinthu za mtengo wake, pamodzi ndi nsembe zaufulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo onse akuwazinga analimbitsa manja ao ndi zipangizo za siliva, ndi golide, ndi chuma, ndi zoweta, ndi zinthu za mtengo wake, pamodzi ndi nsembe zaufulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Onse oyandikana nawo adaŵathandiza poŵapatsa ziŵiya zasiliva, golide, katundu, ziŵeto ndiponso mphatso zamtengowapatali, kuphatikizapo zopereka zija zimene ankazipereka mwaufulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Onse oyandikana nawo anawathandiza powapatsa ziwiya za siliva ndi zagolide, kuphatikizaponso katundu ndi ziweto, ndiponso mphatso zamtengo wapatali, kuwonjezera pa zopereka zaufulu zija. Onani mutuwo |