Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 1:10 - Buku Lopatulika

10 zikho zagolide makumi atatu, zikho zasiliva zina mazana anai ndi khumi, zipangizo zina chikwi chimodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 zikho zagolide makumi atatu, zikho zasiliva zina mazana anai ndi khumi, zipangizo zina chikwi chimodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 timikhate tagolide 30, timikhate tasiliva 2,410, ndi ziŵiya zinanso 1,000.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 timiphika tagolide 230 timiphika tasiliva 410 ziwiya zina 1,000.

Onani mutuwo Koperani




Ezara 1:10
4 Mawu Ofanana  

Zipangizo zonse zagolide ndi zasiliva ndizo zikwi zisanu ndi mazana anai. Izi zonse Sezibazara anakwera nazo, pokwera andende aja kuchokera ku Babiloni kunka ku Yerusalemu.


Kuwerenga kwake ndiko: mbale zagolide makumi atatu, mbale zasiliva chikwi chimodzi, mipeni makumi awiri mphambu isanu ndi inai;


Ndiponso miphika, ndi zoolera, ndi mbano zao, ndi mbale, ndi zipande, ndi zipangizo zonse zamkuwa zimene anatumikira nazo, anazichotsa.


chopereka chake ndicho mbale imodzi yasiliva, kulemera kwake masekeli zana limodzi ndi makumi atatu, mbale yowazira imodzi yasiliva ya masekeli makumi asanu ndi awiri, kuyesa sekeli wa malo opatulika; zonse ziwiri zodzala ndi ufa wosakaniza ndi mafuta, ukhale nsembe yaufa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa