Ezara 1:10 - Buku Lopatulika10 zikho zagolide makumi atatu, zikho zasiliva zina mazana anai ndi khumi, zipangizo zina chikwi chimodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 zikho zagolide makumi atatu, zikho zasiliva zina mazana anai ndi khumi, zipangizo zina chikwi chimodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 timikhate tagolide 30, timikhate tasiliva 2,410, ndi ziŵiya zinanso 1,000. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 timiphika tagolide 230 timiphika tasiliva 410 ziwiya zina 1,000. Onani mutuwo |