Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Estere 8:12 - Buku Lopatulika

12 tsiku lomwelo, m'maiko onse a mfumu Ahasuwero, tsiku lakhumi ndi chitatu la mwezi wakhumi ndi chiwiri, ndiwo mwezi wa Adara.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 tsiku lomwelo, m'maiko onse a mfumu Ahasuwero, tsiku lakhumi ndi chitatu la mwezi wakhumi ndi chiwiri, ndiwo mwezi wa Adara.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Ayuda analoledwa kuchita zimenezi mʼzigawo zonse za Mfumu Ahasiwero pa tsiku limodzi lokha la 13 la mwezi wa 12, mwezi wa Adara.

Onani mutuwo Koperani




Estere 8:12
5 Mawu Ofanana  

Ndipo pokhala mfumu Ahasuwero, poyambira ufumu wake, analembera chowaneneza okhala mu Yuda ndi mu Yerusalemu.


Mwezi wakhumi ndi chiwiri tsono, ndiwo mwezi wa Adara, tsiku lake lakhumi ndi chitatu, mau a mfumu ndi lamulo lake ali pafupi kuchitika, tsikuli adani a Ayuda anayesa kuwachitira ufumu, koma chinasinthika; popeza Ayuda anachitira ufumu iwo odana nao;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa