Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Estere 7:1 - Buku Lopatulika

1 Motero inadza mfumu ndi Hamani kumwa naye mkazi wamkulu Estere.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Motero inadza mfumu ndi Hamani kumwa naye mkazi wamkulu Estere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Choncho mfumu ndi Hamani anabwera kudzadya phwando la mfumukazi Estere.

Onani mutuwo Koperani




Estere 7:1
4 Mawu Ofanana  

Amtokoma anatuluka ofulumizidwa ndi mau a mfumu, ndi lamulo linabukitsidwa m'chinyumba cha ku Susa; ndipo mfumu ndi Hamani anakhala pansi kumwa; koma mzinda wa Susa unadodoma.


ngati mfumu indikomera mtima, ngatinso chakomera mfumu kupereka pempho langa ndi kuchita chofuna ine, adze mfumu ndi Hamani ku madyerero ndidzawakonzera; ndipo mawa ndidzachita monga yanena mfumu.


Akali chilankhulire naye, anafika adindo a mfumu, nafulumira kumtenga Hamani kunka naye kumadyerero adawakonzera Estere.


Nitinso mfumu kwa Estere tsiku lachiwirili pa madyerero a vinyo, Pempho lanu nchiyani, mkazi wamkulu Estere? Lidzapatsidwa kwa inu; mufunanji? Chidzachitika, kufikira limodzi la magawo awiri a ufumu wanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa