Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Estere 5:5 - Buku Lopatulika

5 Niti mfumu, Mumfulumize Hamani, achitike mau a Estere. Nidza mfumu ndi Hamani ku madyerero adawakonzera Estere.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Niti mfumu, Mumfulumize Hamani, achitike mau a Estere. Nidza mfumu ndi Hamani ku madyerero adawakonzera Estere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Mfumu inati, “Muwuzeni abwere Hamani msanga, kotero kuti tichite monga Estere wapempha.” Choncho mfumu ndi Hamani anafika kuphwando limene Estere anakonza.

Onani mutuwo Koperani




Estere 5:5
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Estere anati, Chikakomera mfumu, adze mfumu ndi Hamani lero ku madyerero ndinawakonzera.


Akali chilankhulire naye, anafika adindo a mfumu, nafulumira kumtenga Hamani kunka naye kumadyerero adawakonzera Estere.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa