Estere 5:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Estere anati, Chikakomera mfumu, adze mfumu ndi Hamani lero ku madyerero ndinawakonzera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Estere anati, Chikakomera mfumu, adze mfumu ndi Hamani lero ku madyerero ndinawakonzera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndipo Estere anayankha kuti, “Ngati chingakukomereni, mfumu, mubwere lero pamodzi ndi Hamani kuphwando limene ndakonzera inu mfumu.” Onani mutuwo |