Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Estere 4:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo Mordekai anamfotokozera zonse zidamgwera, ndi mtengo wake wa ndalama adati Hamani adzapereka m'nyumba ya chuma cha mfumu pa Ayuda, kuwaononga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo Mordekai anamfotokozera zonse zidamgwera, ndi mtengo wake wa ndalama adati Hamani adzapereka m'nyumba ya chuma cha mfumu pa Ayuda, kuwaononga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Mordekai anamuwuza zonse zimene zinamuchitikira kuphatikizapo mtengo weniweni wa ndalama zimene Hamani analonjeza kupereka mosungira chuma cha mfumu za anthu amene adzawononge a Yuda.

Onani mutuwo Koperani




Estere 4:7
2 Mawu Ofanana  

Natuluka Hataki kunka kwa Mordekai kukhwalala la mzinda linali popenyana ndi chipata cha mfumu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa