Estere 4:6 - Buku Lopatulika6 Natuluka Hataki kunka kwa Mordekai kukhwalala la mzinda linali popenyana ndi chipata cha mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Natuluka Hataki kunka kwa Mordekai kukhwalala la mudzi linali popenyana ndi chipata cha mfumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Choncho Hataki anapita kwa Mordekai ku bwalo la mzinda patsogolo pa chipata cha mfumu. Onani mutuwo |