Estere 4:2 - Buku Lopatulika2 nafika popenyana ndi chipata cha mfumu; popeza sanathe munthu kulowa kuchipata cha mfumu wovala chiguduli. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 nafika popenyana ndi chipata cha mfumu; popeza sanathe munthu kulowa kuchipata cha mfumu wovala chiguduli. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo anapita ndi kuyima pa chipata cha mfumu, chifukwa panalibe wina aliyense amaloledwa kulowa pa chipata cha mfumu atavala chiguduli. Onani mutuwo |