Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Estere 4:10 - Buku Lopatulika

10 Pamenepo Estere ananena ndi Hataki, namtuma akauze Mordekai, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Pamenepo Estere ananena ndi Hataki, namtuma akauze Mordekai, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ndipo Estere anamutuma Hataki kuti akanene kwa Mordekai kuti,

Onani mutuwo Koperani




Estere 4:10
3 Mawu Ofanana  

Akapolo onse a mfumu ndi anthu a m'maiko a mfumu adziwa kuti aliyense, ngakhale wamwamuna kapena wamkazi, akalowa kwa mfumu kubwalo la m'katimo wosaitanidwa, lamulo la pa iye ndi limodzi, ndilo kuti amuphe, akapanda mfumu kumloza ndi ndodo yachifumu yagolide kuti akhale ndi moyo; koma ine sanandiitane ndilowe kwa mfumu masiku awa makumi atatu.


Pamenepo Estere anaitana Hataki mdindo wina wa mfumu, amene idamuika amtumikire, namuuza amuke kwa Mordekai, kuti adziwe ichi nchiyani ndi chifukwa chake ninji.


Nadza Hataki, namuuza Estere mau a Mordekai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa