Estere 2:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo iye adalera Hadasa, ndiye Estere, mwana wamkazi wa atate wake wamng'ono; popeza iye analibe atate kapena amai; ndi namwaliyo anali wa maonekedwe okoma, ndi wokongola; ndipo atamwalira atate wake ndi mai wake, Mordekai anamtenga akhale mwana wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo iye adalera Hadasa, ndiye Estere, mwana wamkazi wa atate wake wamng'ono; popeza iye analibe atate kapena amai; ndi namwaliyo anali wa maonekedwe okoma, ndi wokongola; ndipo atamwalira atate wake ndi mai wake, Mordekai anamtenga akhale mwana wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Mordekai nʼkuti atalera Hadasa, amene ankatchedwanso Estere, mwana wamkazi wa amalume ake chifukwa analibe abambo kapena amayi. Mtsikanayu anali wokongola ndi wooneka bwino ndipo Mordekai ankamutenga ngati mwana wake weniweni pamene abambo ndi amayi ake anamwalira. Onani mutuwo |