Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Estere 2:2 - Buku Lopatulika

2 Pamenepo anyamata a mfumu omtumikira anati, Amfunire mfumu anamwali okongola;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Pamenepo anyamata a mfumu omtumikira anati, Amfunire mfumu anamwali okongola;

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Tsono anyamata a mfumu amene ankamutumikira anati, “Mfumu, akufunireni anamwali okongola.

Onani mutuwo Koperani




Estere 2:2
6 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene Abramu analowa mu Ejipito, Aejipito anaona kuti mkazi anali wokongola kwambiri.


Pamenepo anyamata ake ananena naye, Amfunire mbuye wanga mfumu namwali, aimirire pamaso pa mfumu namsunge; nagone m'mfukato mwanu, kuti mbuye mfumu yanga afundidwe.


Tsiku lachisanu ndi chiwiri, pokondwera mtima wa mfumu ndi vinyo, iye anauza Mehumani, Bizita, Haribona, Bigita, ndi Abagita, Zetara, ndi Karikasi, adindo asanu ndi awiriwo akutumikira pamaso pa mfumu Ahasuwero,


a pafupi naye ndiwo Karisena, Setara, Adimata, Tarisisi, Meresi, Marisena, ndi Memukana, akalonga asanu ndi awiri a Persiya ndi Mediya, openya nkhope ya mfumu ndi kukhala oyamba mu ufumu.


ndi mfumu aike oyang'anira m'maiko onse a ufumu wake, kuti asonkhanitse anamwali onse okongola m'chinyumba cha ku Susa, m'nyumba ya akazi; awasunge Hegai mdindo wa mfumu wosungira akazi, nawapatse zowayeretsa;


Akali chilankhulire naye, anafika adindo a mfumu, nafulumira kumtenga Hamani kunka naye kumadyerero adawakonzera Estere.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa