Estere 1:2 - Buku Lopatulika2 Masiku ajawo, pokhala Ahasuwero pa mpando wa ufumu wake uli m'chinyumba cha ku Susa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Masiku ajawo, pokhala Ahasuwero pa mpando wa ufumu wake uli m'chinyumba cha ku Susa, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pa nthawi imeneyi nʼkuti mfumu Ahasiwero atakhazikika pa mpando wake wa ufumu mu mzinda wa Susa, Onani mutuwo |