Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 39:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo anapanga mphete ziwiri zagolide, naziika pansonga ziwiri za chapachifuwa, m'mphepete mwake m'katimo, pa mbali ya kuefodi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo anapanga mphete ziwiri zagolide, naziika pa nsonga ziwiri za chapachifuwa, m'mphepete mwake m'katimo, pa mbali ya kuefodi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Adapanga mphete ziŵiri zagolide, nazilumikiza ku nsonga ziŵiri za chovala chapachifuwa cham'mphepete, m'kati mwake, pafupi ndi chovala cha efodi chija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Anapanganso mphete ziwiri zagolide ndipo analumikiza ku ngodya ziwiri zamʼmunsi mwa chovala chapachifuwa, champhepete mwake, mʼkati pafupi ndi efodi ija.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 39:19
3 Mawu Ofanana  

miyala yaberulo, ndi miyala yoika paefodi, ndi pachapachifuwa.


Ndi nsonga zake ziwiri zina za maunyolo awiri opotawo anazimanga pa zoikamo ziwiri, nazimanga pa zapamapewa za efodi, m'tsogolo mwake.


Ndipo anapanga mphete ziwiri zagolide, naziika pa zapamapewa ziwiri za efodi pansi pake, pa mbali yake ya kutsogolo, pafupi pa msoko wake, pamwamba pa mpango wa efodi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa