Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 38:20 - Buku Lopatulika

20 Ndi zichiri zonse za chihema, ndi za bwalo lake pozungulira, nza mkuwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndi zichiri zonse za chihema, ndi za bwalo lake pozungulira, nza mkuwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Koma zikhomo zake za chihema cha Chauta, ndiponso zikhomo zake za bwalolo, zonsezo zinali zamkuŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Zikhomo za chihema ndi zina zonse zozungulira chihemacho zinali zamkuwa.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 38:20
10 Mawu Ofanana  

Ndi kulemera kwake kwa misomali ndiko masekeli makumi asanu a golide. Ndipo anazikuta ndi golide zipinda zosanjikizana.


Ndipo tsopano, kamphindi, Yehova Mulungu wathu wationetsa chisomo, kutisiyira chipulumutso, ndi kutipatsa chichiri m'malo mwake mopatulika; kuti Mulungu wathu atipenyetse m'maso mwathu, ndi kutitsitsimutsa pang'ono mu ukapolo wathu.


Zipangizo zonse za chihema, m'machitidwe ake onse, ndi zichiri zake zonse, ndi zichiri zonse za bwalo lake, zikhale zamkuwa.


Ndi nsichi zake zinali zinai, ndi makamwa ake anai, amkuwa; zokowera zake zasiliva, ndi zokutira mitu yake ndi mitanda yake zasiliva.


Ichi ndi chiwerengo cha zinthu za chihema, chihema cha mboni, monga anaziwerenga, monga mwa mau a Mose, achite nazo Alevi; anaziwerenga Itamara, mwana wa Aroni wansembe.


Mau a anzeru akunga zisonga, omwe akundika mau amene mbusa mmodzi awapatsa mau ao akunga misomali yokhomedwa zolimba.


Ndipo ndidzamkhomera iye ngati chikhomo cholimba; ndipo iye adzakhala mpando wa ulemerero wa banja la atate wake.


Tayang'ana pa Ziyoni, mzinda wa zikondwerero zathu; maso ako adzaona, Yerusalemu malo a phee, chihema chimene sichidzasunthidwa, zichiri zake sizidzazulidwa konse, zingwe zake sizidzadulidwa.


kuchokera kwa Iye amene thupi lonse, lothandizidwa ndi kulumikizidwa pamodzi mwa mfundo ndi mitsempha, likula ndi makulidwe a Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa