Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 36:38 - Buku Lopatulika

38 ndi nsanamira zake zisanu ndi zokowera zao; nakuta mitu yao ndi mitanda yao ndi golide; ndi makamwa ao asanu anali amkuwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 ndi nsanamira zake zisanu ndi zokowera zao; nakuta mitu yao ndi mitanda yao ndi golide; ndi makamwa ao asanu anali amkuwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Tsono adapanga nsanamira zisanu zokhala ndi ngoŵe zokoŵera nsaluyo, ndipo mitu yake ndi mitanda yake adaikuta ndi golide, koma masinde ake anali amkuŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Anapanga nsanamira zisanu ndi ngowe zake. Anakuta pamwamba pa nsanamirazo ndi zomangira zake ndi golide, ndipo anapanganso matsinde asanu amkuwa.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:38
2 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipangira nsalu yotsekerayo nsanamira zisanu za mtengo wakasiya, ndi kuzikuta ndi golide; zokowera zao zikhale zagolide; nuziyengera makamwa asanu amkuwa.


ndi nsichi zake makumi awiri, ndi makamwa ao makumi awiri akhale amkuwa; zokowera za nsichi ndi mitanda yake zikhale zasiliva.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa