Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 36:33 - Buku Lopatulika

33 Ndipo anapititsa mtanda wa pakatipo, pakati pa matabwa kufikira kuthungo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Ndipo anapititsa mtanda wa pakatipo, pakati pa matabwa kufikira kuthungo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Tsono adapanga mtanda wapakati chapakatimpakati, wogwira mafulemuwo kuyambira ku mbali imodzi ya chihema mpaka mbali ina.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Anapanga mtanda wapakati omwe umachokera pa maferemu a mbali ina mpaka mbali inanso.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:33
3 Mawu Ofanana  

Ndi mtanda wa pakati pa matabwa ufikire kuthungo.


ndi mitanda isanu ya matabwa a pa mbali inzake ya chihema, ndi mitanda isanu ya matabwa a chihema ali pa mbali ya kumadzulo.


Ndipo anakuta matabwa ndi golide, napanga mphete zao zagolide zikhale zopisamo mitandayo, nakuta mitandayo ndi golide.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa