Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 35:32 - Buku Lopatulika

32 kulingirira ntchito zaluso, kuchita ndi golide, ndi siliva, ndi mkuwa;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 kulingirira ntchito zaluso, kuchita ndi golide, ndi siliva, ndi mkuwa;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Amadziŵanso kulemba mapulani a ntchito zaluso ndi kugwira ntchito ndi golide, siliva ndi mkuŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Kulemba ndondomeko ya ntchito zaluso ndi kupanga zinthu zagolide, zasiliva ndi zamkuwa,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 35:32
4 Mawu Ofanana  

Uli naonso antchito ochuluka ofukula miyala, ndi amisiri a miyala ndi a mitengo, ndi amuna onse aluso akuchita ntchito zilizonse;


Ndipo uzipanga chihema ndi nsalu zophimba khumi, za bafuta wa thonje losansitsa, ndi thonje lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira; uombemo akerubi, ntchito ya mmisiri.


ndipo anamdzaza ndi mzimu wa Mulungu, ndi luso, ndi nzeru, ndi chidziwitso, za m'ntchito zilizonse;


ndi kuzokota miyala yoikika, ndi kuzokota mitengo, kuchita m'ntchito zilizonse zaluso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa