Eksodo 35:26 - Buku Lopatulika26 Ndi akazi onse ofulumidwa mtima ndi luso anapota ubweyawo wa mbuzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndi akazi onse ofulumidwa mtima ndi luso anapota ubweyawo wa mbuzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Akazi onse alusowo adaombanso nsalu za ubweya wambuzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Ndipo amayi onse amene anali ndi mtima wofuna ndipo anali ndi luso analuka ubweya wa mbuzi. Onani mutuwo |