Eksodo 35:25 - Buku Lopatulika25 Ndi akazi onse a mtima waluso anapota ndi manja ao, nabwera nalo thonje lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndi akazi onse a mtima waluso anapota ndi manja ao, nabwera nalo thonje lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Akazi onse aluso adaomba nsalu za thonje lobiriŵira, lofiirira ndi lofiira. Adabweranso ndi bafuta wa thonje losalala kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Mayi aliyense waluso analuka ndi manja ake ndi kubweretsa chomwe analuka cha mtundu wa mtambo, chapepo kapena chofiira kapena chofewa, chosalala. Onani mutuwo |