Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 35:20 - Buku Lopatulika

20 Ndipo khamu lonse la ana a Israele linachoka pamaso pa Mose.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndipo khamu lonse la ana a Israele linachoka pamaso pa Mose.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Tsono Aisraele onse aja adachoka ndi kumsiya Mose.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Kenaka gulu lonse la Aisraeli linachoka pamaso pa Mose,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 35:20
4 Mawu Ofanana  

Ndipo pobuka mau aja, ana a Israele anapereka mochuluka, zobala zoyamba za tirigu, vinyo, ndi mafuta, ndi uchi, ndi za zipatso zonse za m'minda, ndi limodzi la magawo khumi la zonse anabwera nazo mochuluka.


zovala za kutumikira nazo m'malo opatulika, zovala zopatulika za Aroni wansembe, ndi zovala za ana ake, zakugwira nazo ntchito ya nsembe.


Ndipo anadza, aliyense wofulumidwa mtima, ndi yense mzimu wake wamfunitsa, nabwera nacho chopereka cha Yehova, cha ku ntchito ya chihema chokomanako, ndi ku utumiki wake wonse, ndi ku zovala zopatulika.


Lemekeza Yehova ndi chuma chako, ndi zinthu zako zonse zoyambirira kucha;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa