Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 35:19 - Buku Lopatulika

19 zovala za kutumikira nazo m'malo opatulika, zovala zopatulika za Aroni wansembe, ndi zovala za ana ake, zakugwira nazo ntchito ya nsembe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 zovala za kutumikira nazo m'malo opatulika, zovala zopatulika za Aroni wansembe, ndi zovala za ana ake, zakugwira nazo ntchito ya nsembe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 nsalu zokoma kwambiri zovala anthu otumikira m'malo opatulika, ndiponso zovala zopatulika za wansembe Aroni ndi za ana ake, akamatumikira ngati ansembe.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 zovala zolukidwa zovala potumikira kumalo opatulika, zovala zopatulika za wansembe, Aaroni pamodzi ndi za ana ake aamuna pamene akutumikira monga ansembe.”

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 35:19
7 Mawu Ofanana  

ndi zovala zotumikira nazo, ndi zovala zopatulika za Aroni wansembe, ndi zovala za ana ake, zakuchita nazo ntchito ya nsembe;


zichiri za chihema, ndi zichiri za kubwalo, ndi zingwe zao;


Ndipo khamu lonse la ana a Israele linachoka pamaso pa Mose.


zovala zokoma za kutumikira nazo m'malo opatulika, ndi zovala zopatulika za Aroni wansembe, ndi zovala za ana ake, kuchita nazo ntchito ya nsembe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa