Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 35:17 - Buku Lopatulika

17 nsalu zotchingira za kubwalo, nsichi zake, ndi makamwa ake, ndi nsalu yotsekera ku chipata cha pabwalo;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 nsalu zochingira za kubwalo, nsichi zake, ndi makamwa ake, ndi nsalu yotsekera ku chipata cha pabwalo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 nsalu zochinga bwalo, nsanamira pamodzi ndi masinde ake omwe, nsalu za pa chipata choloŵera ku bwalo,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 nsalu yotchingira bwalo pamodzi ndi mizati yake ndi matsinde ake, ndiponso nsalu yotchingira pa khomo lolowera ku bwalo;

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 35:17
4 Mawu Ofanana  

mfumuyo inanena ndi Natani mneneriyo, Onani ndilikukhala ine m'nyumba yamikungudza, koma likasa la Mulungu lili m'kati mwa nsalu zotchinga.


zichiri za chihema, ndi zichiri za kubwalo, ndi zingwe zao;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa