Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 35:15 - Buku Lopatulika

15 ndi guwa la nsembe lofukizapo, ndi mphiko zake, ndi mafuta odzoza, ndi chofukiza cha fungo lokoma, ndi nsalu yotsekera pakhomo, pa khomo la chihema;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 ndi guwa la nsembe lofukizapo, ndi mphiko zake, ndi mafuta odzoza, ndi chofukiza cha fungo lokoma, ndi nsalu yotsekera pakhomo, pa khomo la Kachisi;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 guwa lofukizirapo lubani ndi mphiko zake, mafuta odzozera, lubani wa fungo lonunkhira bwino, ndiponso nsalu zochingira za pa chipata cha chihema cha Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 guwa lofukizira lubani pamodzi ndi mitengo yake yonyamulira, mafuta odzozera ndi lubani onunkhira; nsalu yotchinga pa khomo lolowera mʼchihema;

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 35:15
6 Mawu Ofanana  

Pemphero langa liikike ngati chofukiza pamaso panu; kukweza manja anga kuikike ngati nsembe ya madzulo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa