Eksodo 29:46 - Buku Lopatulika46 Ndipo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova Mulungu wao, amene ndinawatulutsa m'dziko la Ejipito, kuti ndikhale pakati pao. Ine ndine Yehova Mulungu wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Ndipo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova Mulungu wao, amene ndinawatulutsa m'dziko la Ejipito, kuti ndikhale pakati pao. Ine ndine Yehova Mulungu wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Adzandidziŵa Ine Chauta amene ndidaŵatulutsa ku Ejipito kuti ndikhale pakati pao. Ine ndine Chauta, Mulungu wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Adzadziwa kuti ine ndine Mulungu wawo amene ndinawatulutsa mʼdziko la Igupto kuti ndikhale pakati pawo. Ine ndine Yehova, Mulungu wawo.” Onani mutuwo |