Eksodo 29:45 - Buku Lopatulika45 Ndipo ndidzakhala pakati pa ana a Israele, ndi kukhala Mulungu wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Ndipo ndidzakhala pakati pa ana a Israele, ndi kukhala Mulungu wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 Ndidzakhala pakati pa anthu anga Aisraele, ndipo ndidzakhala Mulungu wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 Ndidzakhala pakati pa Aisraeli ndikukhala Mulungu wawo. Onani mutuwo |
Ndipo anati kwa ine, Wobadwa ndi munthu iwe, pano mpokhala mpando wachifumu wanga, mpoponda kumapazi anga, pomwe ndidzakhala pakati pa ana a Israele kosatha; ndi nyumba ya Israele siidzadetsanso dzina langa loyera, ngakhale iwo kapena mafumu ao, mwa chigololo chao, ndi mitembo ya mafumu ao pa misanje yao,