Eksodo 29:28 - Buku Lopatulika28 ndipo zikhale za Aroni ndi za ana ake aamuna, mwa lemba losatha, ziwadzere kwa ana a Israele; popeza ndiyo nsembe yokweza; ndipo ikhale nsembe yokweza yodzera kwa ana a Israele, ya kwa nsembe zamtendere zao, ndiyo nsembe yao yokweza ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 ndipo zikhale za Aroni ndi za ana ake amuna, mwa lemba losatha, ziwadzere kwa ana a Israele; popeza ndiyo nsembe yokweza; ndipo ikhale nsembe yokweza yodzera kwa ana a Israele, ya kwa nsembe zamtendere zao, ndiyo nsembe yao yokweza ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Pa zimene Aisraele azipereka, zimenezi zikhale za Aroni ndi ana ake nthaŵi zonse. Alandire ndiwo ansembe zonsezi zochokera pa zopereka zamtendere za Aisraele pakuti ndizo mphatso zao za Aisraele kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Nsembe izi ndi zimene Aisraeli azipereka kwa Aaroni ndi ana ake mwa zonse zimene azipereka nthawi zonse. Mwa zopereka za mtendere zimene ana a Aisraeli adzapereka kwa Yehova, zimenezi zikhale gawo lawo. Onani mutuwo |