Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Chivumbulutso 9:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo anali nazo zikopa ngati zikopa zachitsulo; ndipo mkokomo wa mapiko ao ngati mkokomo wa agaleta, a akavalo ambiri akuthamangira kunkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo anali nazo zikopa ngati zikopa zachitsulo; ndipo mkokomo wa mapiko ao ngati mkokomo wa agaleta, a akavalo ambiri akuthamangira kunkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Pachifuwa pake panali mamba onga ngati malaya achitsulo apachifuwa. Kulira kwa mapiko ake kunali ngati kwa magareta ankhondo ambiri okokedwa ndi akavalo othamangira ku nkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Dzombelo linavala za pachifuwa zachitsulo. Phokoso la mapiko awo linali ngati phokoso la magaleta ankhondo ambiri okokedwa ndi akavalo othamangira ku nkhondo.

Onani mutuwo Koperani




Chivumbulutso 9:9
8 Mawu Ofanana  

Pomveka lipenga akuti, Hee! Anunkhiza nkhondo ilikudza kutali, kugunda kwa akazembe ndi kuhahaza.


Mafupa ake akunga misiwe yamkuwa; ziwalo zake zikunga zitsulo zamphumphu.


Pakuti zida zonse za mwamuna wovala zida za nkhondo m'phokosomo, ndi zovala zomvimvinika m'mwazi, zidzakhala zonyeka ngati nkhuni.


Pomveka migugu ya ziboda za olimba ake, pogumukira magaleta ake, ndi pophokosera njinga zake, atate sadzacheukira ana ao chifukwa cha kulefuka kwa manja ao;


Ndipo kotero ndinaona akavalo m'masomphenya, ndi iwo akuwakwera akukhala nazo zikopa za moto, ndi huakinto ndi sulufure; ndi mitu ya akavalo ngati mitu ya mikango; ndipo m'kamwa mwao mutuluka moto ndi utsi ndi sulufure.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa