Chivumbulutso 9:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo anali nalo tsitsi longa tsitsi la akazi, ndipo mano ao anali ngati mano a mikango. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo anali nalo tsitsi longa tsitsi la akazi, ndipo mano ao anali ngati mano a mikango. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsitsi lake linali litalilitali ngati la azimai, mano ake ngati a mkango. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Tsitsi lawo linali ngati la amayi, mano awo ngati a mikango. Onani mutuwo |