Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Chivumbulutso 9:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo anali nalo tsitsi longa tsitsi la akazi, ndipo mano ao anali ngati mano a mikango.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo anali nalo tsitsi longa tsitsi la akazi, ndipo mano ao anali ngati mano a mikango.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Tsitsi lake linali litalilitali ngati la azimai, mano ake ngati a mkango.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Tsitsi lawo linali ngati la amayi, mano awo ngati a mikango.

Onani mutuwo Koperani




Chivumbulutso 9:8
8 Mawu Ofanana  

Ndipo pofika Yehu ku Yezireele, Yezebele anamva, nadzikometsera m'maso, naluka tsitsi lake, nasuzumira pazenera.


Moyo wanga uli pakati pa mikango; ndigona pakati pa oyaka moto, ndiwo ana a anthu amene mano ao ali nthungo ndi mivi, ndipo lilime lao ndilo lupanga lakuthwa.


Ndipo padzakhala m'malo mwa zonunkhiritsa mudzakhala zovunda; ndi m'malo mwa lamba chingwe; ndipo m'malo mwa tsitsi labwino dazi; m'malo mwa chovala chapachifuwa mpango wachiguduli; zipsera m'malo mwa ukoma.


Pakuti mtundu wadza, wakwerera dziko langa, wamphamvu wosawerengeka, mano ake akunga mano a mkango, nukhala nao mano a chibwano a mkango waukulu.


Ndipo monga Yesaya anati kale, Ngati Ambuye wa makamu a kumwamba sanatisiyire ife mbeu, tikadakhala monga Sodomu, ndipo tikadafanana ndi Gomora.


Momwemonso, akazi adziveke okha ndi chovala choyenera, ndi manyazi, ndi chidziletso; osati ndi tsitsi lake loluka, ndi golide kapena ngale, kapena malaya a mtengo wake wapatali;


Amene kukometsera kwanu kusakhale kwa kunja, kuluka tsitsi ndi kuvala za golide, kapena kuvala chovala;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa