Chivumbulutso 9:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo m'masiku ajawo, anthu adzafunafuna imfa osaipeza konse; ndipo adzakhumba kumwalira, koma imfa idzawathawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo m'masiku ajawo, anthu adzafunafuna imfa osaipeza konse; ndipo adzakhumba kumwalira, koma imfa idzawathawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Masiku amenewo anthuwo adzafunafuna imfa, koma osaipeza. Adzafunitsitsa kufa, koma imfa izidzaŵathaŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Masiku amenewo anthu adzafunafuna imfa koma sadzayipeza. Adzalakalaka kufa koma imfa izidzawathawa. Onani mutuwo |